Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 67:1 - Buku Lopatulika

Atichitire chifundo Mulungu, ndi kutidalitsa, atiwalitsire nkhope yake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Atichitire chifundo Mulungu, ndi kutidalitsa, atiwalitsire nkhope yake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu mutikomere mtima ndi kutidalitsa, mutiwunikire ndi chikondi chanu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.

Onani mutuwo



Masalimo 67:1
15 Mawu Ofanana  

Muwalitse nkhope yanu pa mtumiki wanu; ndipo mundiphunzitse malemba anu.


Pulumutsani anthu anu, ndi kudalitsa cholowa chanu; muwawetenso, ndi kuwanyamula nthawi zonse.


Walitsani nkhope yanu pa mtumiki wanu, mundipulumutse ndi chifundo chanu.


Pakufuula ine mundiyankhe, Mulungu wa chilungamo changa; pondichepera mwandikulitsira malo. Ndichitireni chifundo, imvani pemphero langa.


Ambiri amati, Adzationetsa chabwino ndani? Weramutsirani ife kuunika kwa nkhope yanu, Yehova.


Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, ndipo musandilange muukali wanu.


Mulungu adziwika mwa Yuda, dzina lake limveka mwa Israele.


Mutibweze, Yehova Mulungu wa makamu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.


Mulungu wa makamu, mutibweze; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.


Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.


Pakuti Mulungu amene anati, Kuunika kudzawala kutuluka mumdima, ndiye amene anawala m'mitima yathu kutipatsa chiwalitsiro cha chidziwitso cha ulemerero wa Mulungu pankhope pa Yesu Khristu.


Wolemekezeka Mulungu ndi Atate wa Ambuye wathu Yesu Khristu, amene anatidalitsa ife ndi dalitso lonse la mzimu m'zakumwamba mwa Khristu;


Landirani, Yehova, chotetezera anthu anu Israele, amene munawaombola, ndipo musalole mwazi wosachimwa ukhale pakati pa anthu anu Israele; ndipo adzawatetezera cha mwaziwo.