Masalimo 6:1 - Buku Lopatulika1 Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, ndipo musandilange muukali wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, ndipo musandilange m'kukali wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Chauta, musandikalipire ndi kundidzudzula, musapse mtima ndi kundilanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, kapena kundilanga mu ukali wanu. Onani mutuwo |