Masalimo 28:9 - Buku Lopatulika9 Pulumutsani anthu anu, ndi kudalitsa cholowa chanu; muwawetenso, ndi kuwanyamula nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pulumutsani anthu anu, ndi kudalitsa cholandira chanu; muwawetenso, ndi kuwanyamula nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pulumutsani anthu anu, Inu Chauta, mudalitse amene mudaŵasankha. Mukhale mbusa wao, muŵasamale mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu; mukhale mʼbusa wawo ndipo muwakweze kwamuyaya. Onani mutuwo |