Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 29:1 - Buku Lopatulika

1 Perekani kwa Yehova, inu ana a amphamvu, perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Perekani kwa Yehova, inu ana a amphamvu, perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tamandani Chauta, inu okhala kumwamba. Tamandani ulemerero wake ndi mphamvu zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Perekani kwa Yehova, inu anthu amphamvu, perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:1
9 Mawu Ofanana  

Inu Mulungu, ndinu woopsa m'malo oyera anu; Mulungu wa Israele ndiye amene apatsa anthu ake mphamvu ndi chilimbiko. Alemekezeke Mulungu.


Ndiye Mulungu, ayenera kumuopa kwambiri mu upo wa oyera mtima, ndiye wochititsa mantha koposa onse akumzinga.


Pakuti mtundu ndi ufumu umene udzakana kukutumikira udzaonongeka; inde mitundu imeneyo idzasakazidwa ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa