Masalimo 29:2 - Buku Lopatulika2 Perekani kwa Yehova ulemerero wa dzina lake, gwadirani Yehova moyera ndi mokometsetsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Perekani kwa Yehova ulemerero wa dzina lake, gwadirani Yehova moyera ndi mokometsetsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tamandani ulemerero wa dzina la Chauta. Mumpembedze mu ulemu wa ungwiro wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake, pembedzani Yehova mwa kukongola kwa chiyero chake. Onani mutuwo |