Masalimo 4:6 - Buku Lopatulika6 Ambiri amati, Adzationetsa chabwino ndani? Weramutsirani ife kuunika kwa nkhope yanu, Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ambiri amati, Adzationetsa chabwino ndani? Weramutsirani ife kuunika kwa nkhope yanu, Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Alipo ambiri amene amati, “Ndani angatiwonetse zabwino? Mutiyang'ane ndi chikondi chanu, Inu Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?” Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova. Onani mutuwo |