Masalimo 4:7 - Buku Lopatulika7 Mwapatsa chimwemwe mumtima mwanga, chakuposa chao m'nyengo yakuchuluka dzinthu zao ndi vinyo wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Mwapatsa chimwemwe mumtima mwanga, chakuposa chao m'nyengo yakuchuluka dzinthu zao ndi vinyo wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma Inu mwandisangalatsa mtima kwambiri, kupambana anthu a zakudya ndi zakumwa zambiri! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano. Onani mutuwo |