Masalimo 4:8 - Buku Lopatulika8 Ndi mtendere ndidzagona pansi, pomwepo ndidzagona tulo; chifukwa Inu, Yehova, mundikhalitsa ine, ndikhale bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndi mtendere ndidzagona pansi, pomwepo ndidzagona tulo; chifukwa Inu, Yehova, mundikhalitsa ine, ndikhale bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Choncho ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha Chauta ndinu amene mumandisunga bwino lomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha, Inu Yehova, mumandisamalira bwino. Onani mutuwo |