Masalimo 5:1 - Buku Lopatulika1 Mverani mau anga, Yehova, Zindikirani kulingirira kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mverani mau anga, Yehova, Zindikirani kulingirira kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Imvani mau anga, Inu Chauta, mverani kusisima kwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova, ganizirani za kusisima kwanga Onani mutuwo |