Masalimo 5:2 - Buku Lopatulika2 Tamvetsani mau a kufuula kwanga, Mfumu yanga, ndi Mulungu wanga; pakuti kwa Inu ndimapemphera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Tamvetsani mau a kufuula kwanga, Mfumu yanga, ndi Mulungu wanga; pakuti kwa Inu ndimapemphera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Imvani kulira kwanga, Inu Mfumu yanga ndi Mulungu wanga, pakuti ndikupempha chithandizo kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mverani kulira kwanga kofuna thandizo, Mfumu yanga ndi Mulungu wanga, pakuti kwa Inu, ine ndikupemphera. Onani mutuwo |