Masalimo 5:3 - Buku Lopatulika3 M'mawa, Yehova, mudzamva mau anga; m'mawa, ndidzakukonzerani pemphero langa, ndipo ndidzadikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 M'mawa, Yehova, mudzamva mau anga; m'mawa, ndidzakukonzerani pemphero langa, ndipo ndidzadikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 M'maŵa, Inu Chauta, mumamva mau anga. M'maŵa ndimapemphera kwa Inu, ndi kudikira kuti mundiyankhe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mmawa, Yehova mumamva mawu anga; Mmawa ndimayala zopempha zanga pamaso panu ndi kudikira mwachiyembekezo. Onani mutuwo |