Masalimo 4:5 - Buku Lopatulika5 Iphani nsembe za chilungamo, ndipo mumkhulupirire Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Iphani nsembe za chilungamo, ndipo mumkhulupirire Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Perekani nsembe zanu ndi mtima wolungama, ikani mitima yanu pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Perekani nsembe zolungama ndipo dalirani Yehova. Onani mutuwo |