Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 80:7 - Buku Lopatulika

7 Mulungu wa makamu, mutibweze; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Mulungu wa makamu, mutibweze; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Inu Mulungu Wamphamvuzonse, tibwezereni mwakale, mutiwonetse nkhope yoŵala, kuti ife tipulumuke.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Tibwezereni mwakale Inu Mulungu Wamphamvuzonse, nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:7
10 Mawu Ofanana  

Koma Sanibalati Muhoroni, ndi Tobiya kapolo Mwamoniyo, ndi Gesemu Mwarabu, anamva natiseka pwepwete, natipeputsa, nati, Chiyani ichi muchichita? Mulikupandukira mfumu kodi?


Mundilengere mtima woyera, Mulungu; mukonze mzimu wokhazikika m'kati mwanga.


Mutibweze, Yehova Mulungu wa makamu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.


Mutibweze, Mulungu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.


Pakuti atero Ambuye, Yehova Woyera wa Israele, M'kubwera ndi m'kupuma inu mudzapulumutsidwa; m'kukhala chete ndi m'kukhulupirira mudzakhala mphamvu yanu; ndipo simunafune.


Inu mukomana ndi iye amene akondwerera, nachita chilungamo, iwo amene akumbukira Inu m'njira zanu; taonani Inu munakwiya, ndipo ife tinachimwa; takhala momwemo nthawi yambiri, kodi tidzapulumutsidwa?


Iwe Yerusalemu, utsuke mtima wako kuchotsa zoipa kuti upulumuke. Maganizo ako achabe agona mwako masiku angati?


kuti kupenya apenye, koma asazindikire; ndipo kumva amve, koma asadziwitse; kuti pena angatembenuke, ndi kukhululukidwa.


Ndipo iye adzatembenuzira ana a Israele ambiri kwa Ambuye Mulungu wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa