Masalimo 67:2 - Buku Lopatulika2 kuti njira yanu idziwike padziko lapansi, chipulumutso chanu mwa amitundu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kuti njira yanu idziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu mwa amitundu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Njira yanu idziŵike pa dziko lonse lapansi, chipulumutso chanu chidziŵike pakati pa mitundu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse. Onani mutuwo |