Masalimo 67:3 - Buku Lopatulika3 Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu, mitundu yonse ya anthu ikuyamikeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni. Onani mutuwo |