Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 67:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu, mitundu yonse ya anthu ikuyamikeni.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 67:3
8 Mawu Ofanana  

Loleni kuti ndikhale ndi moyo kuti ndikutamandeni, ndipo malamulo anu andichirikize.


Tulutseni mʼndende yanga kuti nditamande dzina lanu. Ndipo anthu olungama adzandizungulira chifukwa cha zabwino zanu pa ine.


Ndidzabukitsa mbiri yako mʼmibado yonse; choncho mitundu yonse idzakutamanda ku nthawi za nthawi.


Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.


Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi; osauka ndi osowa atamande dzina lanu.


Yehovayo tsono akuti, “Nʼchinthu chochepa kwambiri kwa iwe kuti ukhale mtumiki wanga, kuti udzutse mafuko a Yakobo ndi kuwabweretsa kwawo Aisraeli amene anapulumuka. Choncho iwe udzakhala ngati chowunikira, udzafikitsa uthenga wa chipulumutso changa ku mathero a dziko lapansi.”


Nʼchifukwa chake Israeli adzasiyidwa mpaka pa nthawi imene mayi amene ali woyembekezera adzachire. Ndipo abale ake onse otsalira adzabwerera kudzakhala pamodzi ndi Aisraeli.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa