Masalimo 76:1 - Buku Lopatulika1 Mulungu adziwika mwa Yuda, dzina lake limveka mwa Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mulungu adziwika mwa Yuda, dzina lake limveka mwa Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mulungu ndi wodziŵika m'dziko la Yuda, dzina lake ndi lolemekezeka mu Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mulungu amadziwika mu Yuda; dzina lake ndi lotchuka mu Israeli. Onani mutuwo |