Masalimo 80:19 - Buku Lopatulika19 Mutibweze, Yehova Mulungu wa makamu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mutibweze, Yehova Mulungu wa makamu; nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Inu Chauta, Mulungu Wamphamvuzonse, tibwezereni mwakale. Mutiwonetse nkhope yoŵala, kuti ife tipulumuke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe. Onani mutuwo |