Numeri 28:2 - Buku Lopatulika
Uza ana a Israele, nuti nao, Muzisamalira kubwera nacho kwa Ine chopereka changa, chakudya changa cha nsembe zanga zamoto, cha fungo lokoma, pa nyengo yake yoikika.
Onani mutuwo
Uza ana a Israele, nuti nao, Muzisamalira kubwera nacho kwa Ine chopereka changa, chakudya changa cha nsembe zanga zamoto, cha fungo lokoma, pa nyengo yake yoikika.
Onani mutuwo
“Lamula Aisraele, ndipo uŵauze kuti, ‘Muzisamala kupereka kwa Ine pa nthaŵi yake zopereka zanga, chakudya changa cha nsembe yotentha pa moto, yotulutsa fungo londikomera.’
Onani mutuwo
“Lamula Aisraeli kuti, ‘Onetsetsani kuti mukupereka kwa Ine pa nthawi yoyikika, chopereka cha chakudya chotentha pa moto monga fungo lokoma kwa Ine.’
Onani mutuwo