Numeri 15:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo ubwere naye vinyo wa nsembe yothira, limodzi la magawo atatu la hini, achitire Yehova fungo lokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo ubwere naye vinyo wa nsembe yothira, limodzi la magawo atatu la hini, achitire Yehova fungo lokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pachopereka cha chakumwa, mudzapereka vinyo wokwanira lita limodzi ndi theka, kuti ikhale nsembe yotulutsa fungo lokomera Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 ndi vinyo wokwanira lita imodzi ndi theka ngati chopereka cha chakumwa. Muzikapereka monga nsembe yopereka fungo lokoma kwa Yehova. Onani mutuwo |