Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:6 - Buku Lopatulika

6 Kapena ukonzere nkhosa yamphongo nsembe yaufa, awiri mwa magawo khumi a efa wa ufa wosalala, wosakaniza ndi mafuta, limodzi la magawo atatu la hini.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Kapena ukonzere nkhosa yamphongo nsembe yaufa, awiri mwa magawo khumi a efa wa ufa wosalala, wosanganiza ndi mafuta, limodzi la magawo atatu la hini.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Ikakhala nkhosa yamphongo, muzipereka chopereka cha chakudya cholemera makilogaramu aŵiri, wosakaniza ndi mafuta okwanira lita limodzi ndi theka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 “Pamodzi ndi nkhosa yayimuna, muzikakonzanso chopereka cha chakudya cholemera makilogalamu awiri a ufa wosalala, wosakaniza ndi mafuta okwanira lita imodzi ndi theka,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo chopereka chake chikakhala mbuzi, azibwera nayo pamaso pa Yehova;


pamenepo iye wobwera nacho chopereka chake kwa Yehova, azibwera nayo nsembe yaufa, limodzi la magawo khumi la efa wa ufa wosalala, wosakaniza ndi limodzi la magawo anai la hini la mafuta;


ndipo uzikonzera nsembe yopsereza kapena yophera, vinyo wa nsembe yothira, limodzi la magawo anai la hini, ukhale wa mwanawankhosa mmodzi.


Ndipo ubwere naye vinyo wa nsembe yothira, limodzi la magawo atatu la hini, achitire Yehova fungo lokoma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa