2 Akorinto 2:15 - Buku Lopatulika15 Pakuti ife ndife fungo labwino la Khristu, kwa Mulungu, mwa iwo akupulumutsidwa, ndi mwa iwo akuonongeka; kwa ena fungo la imfa kuimfa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pakuti ife ndife fungo labwino la Khristu, kwa Mulungu, mwa iwo akupulumutsidwa, ndi mwa iwo akuonongeka; kwa ena fungo la imfa kuimfa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Zoonadi tili ngati fungo labwino la Khristu lokomera Mulungu, pakati pa anthu amene akupulumuka ndi amene akutayika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pakuti kwa Mulungu ndife fungo labwino la Khristu pakati pa iwo amene akupulumutsidwa ndi amene akuwonongeka. Onani mutuwo |