Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ezara 3:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo anakhazika guwa la nsembe patsinde pake chifukwa cha kuopa iwo anthu a m'maikomo; nakwezera Yehova nsembe zopsereza pamenepo, nsembe zopsereza zam'mawa ndi zamadzulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anakhazika guwa la nsembe patsinde pake chifukwa cha kuopa iwo anthu a m'maikomo; nakwezera Yehova nsembe zopsereza pamenepo, nsembe zopsereza zam'mawa ndi zamadzulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ngakhale kuti ankaopa mitundu ina ya anthu am'maikowo, adamanga guwalo pa maziko ake akale, ndipo ankapereka nsembe zopsereza kwa Chauta paguwapo m'maŵa ndi madzulo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ndi mantha ndi mantha chifukwa cha anthu a mʼmayikomo, iwo anamanga guwalo pa maziko ake akale, ndipo anapereka nsembe zopsereza kwa Mulungu pa guwapo mmawa ndi madzulo.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 3:3
11 Mawu Ofanana  

kupereka nsembe zopsereza kwa Yehova paguwa la nsembe zopsereza, kosalekeza, m'mawa ndi madzulo, monga mwa zonse zilembedwa m'chilamulo cha Yehova adachilamulira Israele;


Anapanganso guwa la nsembe lamkuwa, m'litali mwake mikono makumi awiri, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri, ndi msinkhu wake mikono khumi.


Pamenepo anthu a m'dziko anafoketsa manja a anthu Ayuda, nawavuta pomanga,


nati naye, Tenga zipangizo izi, kaziike mu Kachisi ali mu Yerusalemu, nimangidwe nyumba ya Mulungu pambuto pake.


Ndi pamoto paguwa, m'litali mwake mikono khumi ndi iwiri, ndi kupingasa kwake khumi ndi iwiri, laphwamphwa mbali zake zinai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa