Malaki 1:12 - Buku Lopatulika12 Koma inu muliipsa, pakunena inu, Gome la Ambuye laipsidwa, ndi zipatso zake, chakudya chake, chonyozeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma inu muliipsa, pakunena inu, Gome la Yehova laipsidwa, ndi zipatso zake, chakudya chake, chonyozeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Koma inuyo mumalinyoza ponena kuti tebulo la Chauta nlachabechabe, ndipo chakudya chopereka pamenepo nchonyozeka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Koma inu mumalinyoza ponena kuti tebulo la Ambuye, ‘ndi lodetsedwa,’ ndipo chakudya chake, ‘nʼchonyozeka!’ Onani mutuwo |