Levitiko 3:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo wansembe azitenthe paguwa la nsembe; ndicho chakudya cha nsembe yamoto ya kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo wansembe azitenthe pa guwa la nsembe; ndicho chakudya cha nsembe yamoto ya kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono wansembe atenthe zonsezo pa guwa, kuti zikhale chakudya chotentha pa moto, chopereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Wansembe awotche zonsezi pa guwa. Ichi ndi chakudya chotentha pa moto choperekedwa kwa Yehova. Onani mutuwo |