Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 135:1 - Buku Lopatulika

Aleluya; Lemekezani dzina la Yehova! Lemekezani inu atumiki a Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Aleluya; Lemekezani dzina la Yehova! Lemekezani inu atumiki a Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tamandani Chauta. Tamandani dzina la Chauta, Perekani matamando, inu atumiki a Chauta,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tamandani Yehova. Tamandani dzina la Yehova; mutamandeni, inu atumiki a Yehova,

Onani mutuwo



Masalimo 135:1
18 Mawu Ofanana  

Ndipo maina a ana a Geresomo ndi awa: Libini, ndi Simei.


Nati Alevi, Yesuwa, ndi Kadimiyele, Bani, Hasabineya, Serebiya, Hodiya, Sebaniya, ndi Petahiya, Imirirani, lemekezani Yehova Mulungu wanu kunthawi za nthawi; ndipo lilemekezeke dzina lanu la ulemerero, lokuzika loposa chilemekezo ndi chiyamiko chonse.


Kuti anthu alalikire dzina la Yehova mu Ziyoni, ndi chilemekezo chake mu Yerusalemu;


Aleluya. Yamikani Yehova; pakuti Iye ndiye wabwino: Pakuti chifundo chake nchosatha.


Ayamike Yehova chifukwa cha chifundo chake, ndi zodabwitsa zake za kwa ana a anthu!


Ayamike Yehova chifukwa cha chifundo chake, ndi zodabwitsa zake za kwa ana a anthu!


Aleluya. Ndidzayamika Yehova ndi mtima wonse, mu upo wa oongoka mtima, ndi mumsonkhano.


Aleluya. Wodala munthu wakuopa Yehova, wakukondwera kwambiri ndi malamulo ake.


Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse, akuimirira m'nyumba ya Yehova usiku.


Alemekeze dzina la Yehova; pakuti dzina lake lokha ndi lokwezeka; ulemerero wake uli pamwamba padziko lapansi ndi thambo.


Zonse zakupuma zilemekeze Yehova. Aleluya.


Ndidzayamika Yehova monga mwa chilungamo chake; ndipo ndidzaimbira Yehova Wam'mwambamwamba.