Masalimo 134:3 - Buku Lopatulika3 Yehova, ali mu Ziyoni, akudalitseni; ndiye amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yehova, ali m'Ziyoni, akudalitseni; ndiye amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Akudalitseni Chauta amene amakhala ku Ziyoni, amene adalenga kumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yehova wolenga kumwamba ndi dziko lapansi, akudalitseni kuchokera mʼZiyoni. Onani mutuwo |