Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 134:2 - Buku Lopatulika

2 Kwezani manja anu kumalo oyera, nimulemekeze Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Kwezani manja anu kumalo oyera, nimulemekeze Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Kwezani manja anu popemphera m'malo ake oyera, ndipo mutamande Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Kwezani manja anu mʼmalo opatulika ndipo mutamande Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 134:2
10 Mawu Ofanana  

Pamenepo Ezara analemekeza Yehova Mulungu wamkulu. Navomereza anthu onse, ndi kuti, Amen, Amen; nakweza manja ao, nawerama, nalambira Yehova nkhope zao pansi.


Pemphero langa liikike ngati chofukiza pamaso panu; kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo.


Ndidzasamba manja anga mosalakwa; kuti ndizungulire guwa la nsembe lanu, Yehova;


Mverani mau a kupemba kwanga, pamene ndilirira Inu, pamene ndikweza manja anga kuloza ponenera panu poyera.


Kuti ndione mphamvu yanu ndi ulemerero wanu, monga ndinakuonani m'malo oyera.


Potero ndidzakuyamikani m'moyo mwanga; ndidzakweza manja anga m'dzina lanu.


Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi zonona; ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakufuula mokondwera.


Tauka, tafuula usiku, poyamba kulonda; tsanulira mtima wako ngati madzi pamaso pa Ambuye; takwezera maso ako kwa Iye, chifukwa cha moyo wa tiana tako, timene tilefuka ndi njala pa malekezero a makwalala onse.


Titukulire mitima yathu ndi manja athu omwe kwa Mulungu ali kumwamba.


Chifukwa chake ndifuna kuti amunawo apemphere pamalo ponse, ndi kukweza manja oyera, opanda mkwiyo ndi makani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa