Masalimo 134:1 - Buku Lopatulika1 Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse, akuimirira m'nyumba ya Yehova usiku. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse, akuimirira m'nyumba ya Yehova usiku. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Bwerani, mudzatamande Chauta, Inu nonse atumiki a Chauta, inu amene mumatumikira m'Nyumba mwake usiku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Bwerani, mutamande Yehova, inu atumiki onse a Yehova, amene mumatumikira usiku mʼnyumba ya Yehova. Onani mutuwo |