Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 150:6 - Buku Lopatulika

6 Zonse zakupuma zilemekeze Yehova. Aleluya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Zonse zakupuma zilemekeze Yehova. Aleluya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Chauta. Tamandani Chauta!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 150:6
7 Mawu Ofanana  

Lemekezani Yehova, inu, ntchito zake zonse, ponseponse pali ufumu wake: Lemekeza Yehova, moyo wanga iwe.


Ntchito zanu zonse zidzakuyamikani, Yehova; ndi okondedwa anu adzakulemekezani.


Pakamwa panga padzanena chilemekezo cha Yehova; ndi zinthu zonse zilemekeze dzina lake loyera kunthawi za nthawi.


Alemekeze dzina la Yehova; pakuti dzina lake lokha ndi lokwezeka; ulemerero wake uli pamwamba padziko lapansi ndi thambo.


Mulungu, mokhala mwake moyera, ndiye Atate wa ana amasiye, ndi woweruza wa akazi amasiye.


Ndipo cholengedwa chilichonse chili m'mwamba, ndi padziko, ndi pansi padziko, ndi m'nyanja, ndi zonse zili momwemo, ndinazimva zilikunena, Kwa Iye wakukhala pa mpando wachifumu, ndi kwa Mwanawankhosa zikhale chiyamiko, ndi ulemu, ndi ulemerero, ndi mphamvu, kufikira nthawi za nthawi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa