Masalimo 107:8 - Buku Lopatulika8 Ayamike Yehova chifukwa cha chifundo chake, ndi zodabwitsa zake za kwa ana a anthu! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ayamike Yehova chifukwa cha chifundo chake, ndi zodabwitsa zake za kwa ana a anthu! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Athokoze Chauta chifukwa cha chikondi chake chosasinthika, chifukwa cha ntchito zake zodabwitsa kwa anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha ndi chifukwa cha machitidwe ake odabwitsa kwa anthu onse, Onani mutuwo |