Masalimo 148:13 - Buku Lopatulika13 Alemekeze dzina la Yehova; pakuti dzina lake lokha ndi lokwezeka; ulemerero wake uli pamwamba padziko lapansi ndi thambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Alemekeze dzina la Yehova; pakuti dzina lake lokha ndi lokwezeka; ulemerero wake uli pamwamba pa dziko lapansi ndi thambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Onsewo atamande dzina la Chauta, pakuti dzina lake lokha nlolemekezeka, ulemerero wake ndi woposa, pansi pano nkumwamba komwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Onsewo atamande dzina la Yehova pakuti dzina lake lokha ndi lolemekezeka; ulemerero wake ndi woopsa pa dziko lapansi pano ndi kumwamba komwe. Onani mutuwo |