Masalimo 148:12 - Buku Lopatulika12 Anyamata ndiponso anamwali; okalamba pamodzi ndi ana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Anyamata ndiponso anamwali; okalamba pamodzi ndi ana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu anyamata pamodzi ndi anamwali, inu nkhalamba ndi ana omwe! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Inu anyamata ndi anamwali, inu nkhalamba ndi ana omwe. Onani mutuwo |