Masalimo 148:11 - Buku Lopatulika11 Mafumu a padziko ndi mitundu yonse ya anthu; zinduna ndi oweruza onse a padziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mafumu a padziko ndi mitundu yonse ya anthu; zinduna ndi oweruza onse a padziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Inu mafumu a pa dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse, inu akuluakulu ndi olamulira dziko lapansi! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Inu mafumu a dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse, inu akalonga ndi olamulira a dziko lapansi. Onani mutuwo |