Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 99:2 - Buku Lopatulika

Yehova ndiye wamkulu mu Ziyoni; ndipo akwezeka pamwamba pa mitundu yonse ya anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova ndiye wamkulu m'Ziyoni; ndipo akwezeka pamwamba pa mitundu yonse ya anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta ndi wamkulu ku Ziyoni. Ali pamwamba pa mitundu yonse ya anthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mʼziyoni wamkulu ndi Yehova; Iye ndi wokwezeka pamwamba pa mitundu yonse ya anthu.

Onani mutuwo



Masalimo 99:2
15 Mawu Ofanana  

Yehova akwezeka pamwamba pa amitundu onse, ulemerero wake pamwambamwamba.


Atigonjetsera anthu, naika amitundu pansi pa mapazi athu.


Mulungu ndiye mfumu ya amitundu, Mulungu akhala pa mpando wachifumu wake woyera.


Mulungu awalira mu Ziyoni, mokongola mwangwiro.


Achita ufumu mwa mphamvu yake kosatha; maso ake ayang'anira amitundu; opikisana ndi Iye asadzikuze.


Pakuti Inu, Yehova, ndinu Wam'mwambamwamba padziko lonse lapansi, ndinu wokwezeka kwakukulu pamwamba pa milungu ina yonse.


Tafuula, takuwa iwe, wokhala mu Ziyoni, chifukwa Woyera wa Israele wa m'kati mwako ali wamkulu.


Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ake ovutidwa adzaona pobisalira.


Sayang'anira mphulupulu ili mu Yakobo, kapena sapenya kupulukira kuli mu Israele. Yehova Mulungu wake ali ndi iye, ndi mfuu wa mfumu uli pakati pao.