Masalimo 47:8 - Buku Lopatulika8 Mulungu ndiye mfumu ya amitundu, Mulungu akhala pa mpando wachifumu wake woyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mulungu ndiye mfumu ya amitundu, Mulungu akhala pa mpando wachifumu wake woyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mulungu amalamulira mitundu ya anthu. Mulungu amakhala pa mpando wake woyera waufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mulungu akulamulira mitundu ya anthu; Mulungu wakhala pa mpando wake waufumu woyera. Onani mutuwo |