Masalimo 47:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti Mulungu ndiye mfumu ya dziko lonse lapansi; imbirani ndi chilangizo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti Mulungu ndiye mfumu ya dziko lonse lapansi; imbirani ndi chilangizo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mulungu ndiye Mfumu ya dziko lonse lapansi. Imbani mwaluso nyimbo zotamanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi; imbirani Iye salimo la matamando. Onani mutuwo |