Masalimo 47:9 - Buku Lopatulika9 Akulu a anthu asonkhana akhale anthu a Mulungu wa Abrahamu, pakuti zikopa za dziko lapansi nza Mulungu; akwezeka kwakukulu Iyeyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Akulu a anthu asonkhana akhale anthu a Mulungu wa Abrahamu, pakuti zikopa za dziko lapansi nza Mulungu; akwezeka kwakukulu Iyeyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Atsogoleri a anthu a mitundu ina yonse amasonkhana pamodzi ndi anthu a Mulungu wa Abrahamu, pakuti mafumu onse a pansi pano ndi ake a Mulungu, Iyeyo ndiye wamkulu kopambana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana monga anthu a Mulungu wa Abrahamu, pakuti mafumu a dziko lapansi ndi ake a Mulungu; Iye wakwezedwa kwakukulu. Onani mutuwo |