Masalimo 48:1 - Buku Lopatulika1 Yehova ndiye wamkulu, ayenera kulemekezekadi, m'mzinda wa Mulungu wathu, m'phiri lake loyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova ndiye wamkulu, ayenera kulemekezekadi, m'mudzi wa Mulungu wathu, m'phiri lake loyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta ndi wamkulu, ndi woyenera kumutamanda kwambiri. Timuyamike mu mzinda wake, pa phiri lake loyera, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera. Onani mutuwo |