Masalimo 113:4 - Buku Lopatulika4 Yehova akwezeka pamwamba pa amitundu onse, ulemerero wake pamwambamwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Yehova akwezeka pamwamba pa amitundu onse, ulemerero wake pamwambamwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta akulamulira anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi waukulu kuposa wa mlengalenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi woposa mayiko akumwamba. Onani mutuwo |