Masalimo 113:5 - Buku Lopatulika5 Akunga Yehova Mulungu wathu ndani? Amene akhala pamwamba patali, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Akunga Yehova Mulungu wathu ndani? Amene akhala pamwamba patali, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndani angalingane ndi Chauta, Mulungu wathu, amene akukhala kumwamba, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba? Onani mutuwo |