Masalimo 113:3 - Buku Lopatulika3 Chitulukire dzuwa kufikira kulowa kwake lilemekezedwe dzina la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chitulukire dzuwa kufikira kulowa kwake lilemekezedwe dzina la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Dzina la Chauta litamandike kuyambira ku matulukiro a dzuŵa mpaka ku maloŵero ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake, dzina la Yehova liyenera kutamandidwa. Onani mutuwo |