Masalimo 66:7 - Buku Lopatulika7 Achita ufumu mwa mphamvu yake kosatha; maso ake ayang'anira amitundu; opikisana ndi Iye asadzikuze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Achita ufumu mwa mphamvu yake kosatha; maso ake ayang'anira amitundu; opikisana ndi Iye asadzikuze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Iye amalamula ndi mphamvu zake mpaka muyaya, maso ake amalonda mitundu ina ya anthu. Anthu oukira asadzikweze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye amalamulira ndi mphamvu zake mpaka muyaya, maso ake amayangʼanira anthu a mitundu ina. Anthu owukira asadzitukumule. Onani mutuwo |