Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 66:8 - Buku Lopatulika

8 Lemekezani Mulungu wathu, mitundu ya anthu inu, ndipo mumveketse liu la chilemekezo chake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Lemekezani Mulungu wathu, mitundu ya anthu inu, ndipo mumveketse liu la chilemekezo chake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Lemekezani Mulungu wathu, inu mitundu ya anthunu, mau omtamanda Iye amveke.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Tamandani Mulungu wathu, inu mitundu ya anthu, mulole kuti mawu a matamando ake amveke;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 66:8
9 Mawu Ofanana  

Ombani m'manja, mitundu yonse ya anthu; fuulirani kwa Mulungu ndi liu la kuimbitsa.


Imbirani ulemerero wa dzina lake; pomlemekeza mumchitire ulemerero.


Fuulirani kwa Yehova, inu, dziko lonse lapansi; kuwitsani ndi kufuulira mokondwera; inde, imbirani zomlemekeza.


mudzamvekanso mau akukondwa ndi mau akusekera, mau a mkwati ndi mau a mkwatibwi, mau a iwo akuti, Myamikireni Yehova wa makamu, pakuti Yehova ndiye wabwino, chifundo chake nchosatha; ndi a iwo akutengera nsembe zoyamikira m'nyumba ya Yehova. Pakuti ndidzabweza undende wa dziko monga poyamba, ati Yehova.


Kondwerani, amitundu inu, ndi anthu ake; adzalipsira mwazi wa atumiki ake, adzabwezera chilango akumuukira, nadzafafanizira zoipa dziko lake, ndi anthu ake.


Zitatha izi ndinamva ngati mau aakulu a khamu lalikulu mu Mwamba, lili kunena, Aleluya; chipulumutso, ndi ulemerero, ndi mphamvu, nza Mulungu wathu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa