Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 66:9 - Buku Lopatulika

9 Iye amene asunga moyo wathu tingafe, osalola phazi lathu literereke.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Iye amene asunga moyo wathu tingafe, osalola phazi lathu literereke.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Iye watchinjiriza moyo wathu, sadalole kuti mapazi athu aterereke.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iye watchinjiriza miyoyo yathu ndi kusunga mapazi athu kuti angaterereke.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 66:9
13 Mawu Ofanana  

Popeza sadzagwedezeka nthawi zonse; wolungama adzakumbukika ku nthawi yosatha.


Sadzalola phazi lako literereke: Iye amene akusunga sadzaodzera.


Pakuti ndodo yachifumu ya choipa siidzapumula pa gawo la olungama; kuti olungama asatulutse dzanja lao kuchita chosalungama.


Onenepa onse a padziko lapansi adzadya nadzagwadira; onse akutsikira kufumbi adzawerama pamaso pake, ndi iye amene sadziwa kusunga moyo wake.


Koma Inu, Mulungu, mudzawatsitsira kudzenje la chionongeko. Anthu okhetsa mwazi ndi achinyengo masiku ao sadzafikira nusu; koma ine ndidzakhulupirira Inu.


Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; msanje wanga, sindidzagwedezeka kwakukulu.


Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa, msanje wanga, sindidzagwedezeka.


Pamene ndinati, Literereka phazi langa, chifundo chanu, Yehova, chinandichirikiza.


pakuti mwa Iye tikhala ndi moyo ndi kuyendayenda, ndi kupeza mkhalidwe wathu; monga enanso a akuimba anu ati, Pakuti ifenso tili mbadwa zake.


Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu.


Ngakhale anauka anthu kukulondolani, ndi kufuna moyo wanu, koma moyo wa mbuye wanga udzamangika m'phukusi la amoyo lakukhala ndi Yehova Mulungu wanu; koma Iye adzaponya miyoyo ya adani anu kuwataya monga chotuluka m'choponyera mwala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa