Masalimo 66:9 - Buku Lopatulika9 Iye amene asunga moyo wathu tingafe, osalola phazi lathu literereke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Iye amene asunga moyo wathu tingafe, osalola phazi lathu literereke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Iye watchinjiriza moyo wathu, sadalole kuti mapazi athu aterereke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye watchinjiriza miyoyo yathu ndi kusunga mapazi athu kuti angaterereke. Onani mutuwo |