Masalimo 99:3 - Buku Lopatulika3 Alemekeze dzina lanu lalikulu ndi loopsa. Ili ndilo loyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Alemekeze dzina lanu lalikulu ndi loopsa. Ili ndilo loyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Onse atamande dzina lake lalikulu ndi loopsa! Iye ndi woyera! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anthu atamande dzina lanu lalikulu ndi loopsa kwambiri, Iye ndi woyera. Onani mutuwo |
Ndipo tsono, Mulungu wathu, ndinu Mulungu wamkulu, ndi wamphamvu, ndi woopsa, wakusunga pangano ndi chifundo, asachepe pamaso panu mavuto athu onse amene anatigwera ife, ndi mafumu athu, akulu athu, ndi ansembe athu, ndi aneneri athu, ndi makolo athu, ndi anthu anu onse, kuyambira masiku a mafumu a Asiriya, mpaka lero lino.