Masalimo 99:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anthu atamande dzina lanu lalikulu ndi loopsa kwambiri, Iye ndi woyera. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Alemekeze dzina lanu lalikulu ndi loopsa. Ili ndilo loyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Alemekeze dzina lanu lalikulu ndi loopsa. Ili ndilo loyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Onse atamande dzina lake lalikulu ndi loopsa! Iye ndi woyera! Onani mutuwo |
“Nʼchifukwa chake, tsono, Inu Mulungu wathu, Mulungu wamkulu, wamphamvu ndi woopsa kwambiri mumasunga pangano ndi chikondi chosasinthika. Musalole kuti mavuto onse amene atigwera ife, mafumu athu, atsogoleri athu, ansembe athu, aneneri athu, makolo athu ndi anthu ena onse kuyambira nthawi ya mafumu a ku Asiriya mpaka lero aoneke ochepa pamaso panu.