Masalimo 99:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo mphamvu ya mfumu ikonda chiweruzo; Inu mukhazikitsa zolunjika, muchita chiweruzo ndi chilungamo mu Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo mphamvu ya mfumu ikonda chiweruzo; Inu mukhazikitsa zolunjika, muchita chiweruzo ndi chilungamo m'Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndinu Mfumu yamphamvu, yokonda chilungamo, mwakhazikitsa khalidwe losakondera ndiponso kuweruza kolungama m'dziko la Yakobe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mfumu yamphamvu, iyo imakonda chilungamo Inu mwakhazikitsa khalidwe losakondera; mwachita zolungama ndi zoyenera mwa Yakobo. Onani mutuwo |