Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 143:4 - Buku Lopatulika

Potero mzimu wanga wakomoka mwa ine; mtima wanga utenga nkhawa m'kati mwanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Potero mzimu wanga wakomoka mwa ine; mtima wanga utenga nkhawa m'kati mwanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake mtima wanga wafooka m'kati mwanga, mumtima mwangamu mukuchita mantha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga; mʼkati mwanga, mtima wanga uli ndi nkhawa.

Onani mutuwo



Masalimo 143:4
13 Mawu Ofanana  

Indetu, mugwetsera wamasiye msampha, mumkumbira bwenzi lanu mbuna.


Yehova, imvani pemphero langa, ndipo mfuu wanga ufikire Inu.


Akadatimiza madziwo, mtsinje ukadapita pa moyo wathu;


Pamene mzimu wanga unakomoka m'kati mwanga, munadziwa njira yanga. M'njira ndiyendamo ananditchera msampha.


Penyani kudzanja lamanja ndipo muone; palibe wondidziwa; pothawirapo pandisowa; palibe mmodzi wosamalira moyo wanga.


Cheukirani ine ndipo ndichitireni chifundo; pakuti ndili wounguluma ndi wozunzika.


Mantha ndi kunjenjemera zandidzera, ndipo zoopsetsa zandikuta.


Ku malekezero a dziko lapansi ndidzafuulira kwa Inu, pomizika mtima wanga. Nditsogolereni kuthanthwe londiposa ine m'kutalika kwake.


Ndikumbukira Mulungu ndipo ndivutika; ndilingalira ndipo mzimu wanga ukomoka.


Ndikumbukira nyimbo yanga usiku; ndilingalira mumtima mwanga; mzimu wanga unasanthula.


Ndipo pokhala Iye m'chipsinjo mtima anapemphera kolimba koposa ndithu: ndi thukuta lake linakhala ngati madontho aakulu a mwazi alinkugwa pansi.