Masalimo 143:5 - Buku Lopatulika5 Ndikumbukira masiku a kale lomwe; zija mudazichita ndilingirirapo; ndikamba pandekha za ntchito ya manja anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndikumbukira masiku a kale lomwe; zija mudazichita ndilingirirapo; ndikamba pandekha za ntchito ya manja anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndimakumbukira masiku amakedzana, ndimasinkhasinkha za zonse zimene mwazichita, ndimalingalira ntchito za manja anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndimakumbukira masiku amakedzana; ndimalingalira za ntchito yanu yonse, ndimaganizira zimene manja anu anachita. Onani mutuwo |